Tuesday, December 23, 2025
No menu items!
spot_img
Home Blog Page 1132

A DPP akufuna kubweletsa chisokonezo poyika m’bale wathu Saulos Chilima- Zatero Mbadwa Zokhudzidwa

0

By Joseph Banda

Gulu lina lomwe likuzitchula kuti ‘Mbadwa Zokhudzidwa’ lati chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) chamema achinyamata ena omwe chikufuna kuti akayambitse chisokonezo mawa lino pa mwambo oyika m’manda thupi la yemwe anali wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko Dr. Saulos Chilima kumudzi kwawo ku Ntcheu.

Kudzera mchikalata chomwe ife taona, gululi lati lili ndi umboni onse pa izi.

“Ife monga Mbadwa Zokhudzidwa, tikufuna kuima pamodzi ndi mtundu onse wa Malawi pamodzi ndi Mtsogoleri wa dziko lino Dr. Lazarus Chakwera polira abale ndi alongo Including the Vice President Rt. Honourable Dr Saulos Klaus Chilima, amene ataya miyoyo yawo pangozi ija ya ndenge imene idachitika pa 10 June 2025 Ku Chikangawa.

Mbadwa zokhudzidwa



“Ife Mbadwa Zokhudzidwa tapezapo zinthu zingapo zimene ngati sitingalankhulepo ndiye kuti sitichita bwino pofuna kulemekeza moyo ndi Khalidwe la Dr. Saulos Klaus Chilima zomwe adaonesa pokhala dziko lapansi lino.

“Ndizomvetsa chisoni komanso zochititsa manyazi kuti pali anthu ena andale, maka maka a DPP omwe akufuna kutchukilapo pa maliro a Saulos Chilima. Tilinawo umboni okwanila ndipo tikudziwa anthu onse a DPP omwe akupereka ndalama kwa anyamata kuti akanyazitse President Chakwera ku maliro a Chilima ku Nsipe mawa.

“Tawawona akujijilika ku siwa kufuna kukhala ngati kuti amamukonda Saulos pomwe ndiwomwewa amamunyoza, kumunyazitsa, kumutukwana Saulos.

“Pano watisiya, akufuna akhale angelo.
Ife ngati Mbadwa Zokhudzidwa tapeza kuti azipani zotsutsa afuna kuti apangirepo ndale zawo pa Maliro amene agwera dziko lino,” latero gululi mchikalata chake.

Gululi lati laonapo ma audio clip akutuluka kuchokera kwa a  Ntanyiwa a Limpopo FM omwe amakhalira ku dziko la South Africa namakamba nkhani zamabodza ndikufuna kuononga mbiri ya anthu ena kuphatikizapo mtsogoleri wadziko lino motumidwa ndi a zipani zotsutsa amene amakatengako ndalama kudzera kwa munthu wina amene amakhala ku South Africa koma adali mugawo limodzi la chitetezo Cha Mtsogoleri wakale  wadziko lino  Prof Arthur Peter Mutharika.

“Iyeyo amalumikiza ma wire pakati pa anthu aku DPP ndi Limpopo FM.
Anthuwa akungofuna kudzetsa mkwiyo kwa mzika za Malawi ponena zinthu za mkutu. Mbadwa Zokhudzidwa zapeza kuti a zipani zotsutsa ndiwo akhala akukolezera kuti a Chipani Cha UTM azipanga zithu mokwiya poperekera zida kuti anthu adziyimba nyimbo zonyoza a Chakwera zomwe sizingakondwereste mzimu wa Dr. Chilima.

“Dr. Chilima adali mkatolika weni weni osachita nawo mapokoso opanda mzeru.

“Mbadwa Zokhudzidwa zapeza kuti a zipani zotsutsa apeza njira yofuna kutchukirapo muzipani zawo pofuna kubweresa mabodza ochuluka kuti anthu adane ndi a Chakwera.

“Tamva kuti akufuna kuti a Peter Mutharika akapita ku maliro asakagwirane chanza ndi aliyense kapena kumwa madzi amene akapatsidwe ati angakawaphe. Za ziii zeni zeni. Mutharika amapita ku maliro?

“Tikudziwa kuti zonsenzi mkufuna kupeza zifukwa zoti asakapezeke ku Maliro a Dr. Chilima. Koma a Malawi akudziwa kale kuti inu simupita ku Maliro,” chaonjezera chotele chikalatachi.

Ndipo chapitiliza kunena kuti :”Imfa ya Dr.Justin Malewezi amene adakhalapo Vice President wa dziko lino la Malawi mu utsogoleri wa Dr. Bakili Muluzi APM adabwera?

“Maliro a mayi Annie Muluzi Mayi awo a Dr. Atupele Muluzi, amene adali running mate wanu mu 2019, mudabwera?

“Maliro Vice President wanu Dr. Goodal Gondwe, mudakakamizidwa tsiku lomaliza pomwenso mudakafika mochedwa osawona nkhope.

“Maliro senior chiefs mdziko muno including a Chimaliro aku Thyolo kumene amacholera APM, mudapita?  Mdziko muno mudachitika maliro a senior Chief Kapoloma amene adali related to former President wa dziko lino Dr Bakili Muluzi ku Liwonde koma a Peter Mutharika okhalira ku Mangochi sadapezeke so.

“Chimene chikhale chachilendo ndi chiti kuti APM akalephere kupita ku maliro a Dr Klaus Chilima

“Dr Saulos Klaus Chilima sadali munthu amene amachitidwa provoke so easily and react to carelessly.

“Mulemekezeni. Wakhala moyo wa chete kuchokera pamene Chipani Cha DPP chidakhala chikumuchita provoke. Mwachitsanzo adayankhapo munthawi Ina pamene a DPP adamuyamba ndikunena kuti iye ngosayamika.
Adayankha nanena kuti musati ndine osayamika chifukwa sindikuyenera kukhala ineyo okuyamikani chifukwa ndidakupezani ku opposition ndikukulowetsani m’boma, so mukuyenera kundiyamika ndi Inuyo.

“A DPP adamuchita provoke namanena kuti adamutenga akugulitsa yabooka ndipo amutsuka tsuka. A DPP adatenga mzimayi amene adachita video clip nkuwuza anthu kuti Dr. Saulos Klaus Chilima sadali wa ku Ntcheu koma ku Mozambique.

“Ndipo a DPP adamutchula kuti Iye ndi Zeze not Saulos Klaus Chilima.
Wakoma lero Saulos mumamunyoza uja? Chonde a Malawi a mzanga maka uko ku Ntcheu a Ngoni, tisalore kuti anthu a DPP atigwiritse ntchito yosokoneza maliro a Dr. Chilima.

“Mulemekezeni m’bale wanu kuti mzimu wake uwuse mu mtendere.”

DPP Spokesperson dismiss fake letters to AFORD President Enoch Chihana

0


By Burnett Munthali


Tensions in Malawi’s political scene have escalated following the Democratic Progressive Party’s (DPP) strong denouncement of letters allegedly authored by the Malawi Congress Party (MCP). These letters purportedly warned AFORD President Enoch Chihana about potential actions that could undermine MCP’s political interests. This controversy underscores the intricacies of political maneuvering and alliances as parties gear up for future electoral battles.


Both the DPP presidential candidate and spokesperson have vehemently criticized the letters attributed to MCP. They dismiss them as manipulative attempts to interfere in AFORD’s internal affairs and sow discord among opposition parties. According to DPP officials, such tactics not only jeopardize the spirit of fair competition but also undermine efforts to build a united front against the ruling party.

Namalomba

DPP representatives have framed MCP’s alleged actions as indicative of desperation to consolidate power and influence within opposition ranks. They argue that these maneuvers aim to weaken solidarity among opposition parties, thereby potentially benefiting the ruling party in upcoming elections.

The controversy has sparked diverse reactions from the public and political observers. Supporters of MCP may see the letters as legitimate efforts to protect party interests, while critics view them as divisive and detrimental to broader opposition unity. The incident has prompted calls for transparency and ethical conduct in political engagements to uphold democratic principles.


As Malawi approaches future elections, the fallout from this controversy could shape electoral strategies and alliances. It underscores the complexities of coalition-building and strategic positioning among political parties, influencing voter perceptions and potential outcomes at the ballot box.


The DPP’s dismissal of MCP’s warning letters to AFORD President Enoch Chihana highlights the competitive nature of Malawi’s political landscape. As parties navigate these challenges, maintaining integrity, fostering unity, and adhering to democratic norms will be crucial in shaping the country’s political future. The unfolding dynamics will continue to shape the narrative leading up to the next electoral cycle, impacting the choices and outcomes for Malawian voters.

Tanzanian VP Philip Mpango Reflects on VP Saulos Chilima: A Tribute of Respect and Admiration

0


By Burnett Munthali

Vice President Saulos Chilima of Malawi left an enduring impression not only on his own nation but also on regional counterparts, including Tanzanian Vice President Philip Mpango. In a heartfelt reflection, Mpango offered insights into the character, leadership, and legacy of Vice President Chilima, highlighting his impact beyond borders on Sunday 16 June 2024 at Bingu Stadium in Lilongwe.

Vice President Mpango began by recounting his initial interactions with Saulos Chilima, describing him as a visionary leader whose early career in economics and corporate governance set a strong foundation for his subsequent political journey. He praised Chilima’s achievements in the private sector, noting their resonance in his approach to public service.

Mpango Speaking at Chilima funeral



Highlighting their shared commitment to regional integration and economic cooperation, Vice President Mpango emphasized Chilima’s role in promoting bilateral relations between Malawi and Tanzania. He acknowledged Chilima’s efforts in fostering dialogue and collaboration on issues of mutual interest, which contributed to strengthening ties between the two nations.

Vice President Mpango spoke admiringly of Chilima’s leadership style, characterized by integrity, diligence, and a deep sense of responsibility towards his nation and its people. He lauded Chilima’s unwavering dedication to transparency and accountability, which earned him respect both domestically and internationally.

Reflecting on Chilima’s tenure as Vice President, Mpango highlighted his significant contributions to governance reforms in Malawi. He praised Chilima’s initiatives aimed at enhancing efficiency, combating corruption, and improving public service delivery, noting their transformative impact on Malawian society.

In a personal tribute, Vice President Mpango shared anecdotes that underscored Chilima’s humility, compassion, and dedication to uplifting others. He recalled moments of shared camaraderie and mutual respect, which deepened their professional relationship and friendship over the years.


Vice President Philip Mpango’s reflection on Vice President Saulos Chilima serves as a poignant testament to the admiration and respect he garnered not only in Malawi but also among regional peers. As Malawi continues to honor the legacy of Saulos Chilima, Vice President Mpango’s tribute underscores the enduring impact of leadership driven by vision, integrity, and a commitment to advancing the common good.

Chakwera assures Malawi VP Chilima’s accident will be thoroughly investigated

0

By Staff Reporter

His Excellency, Dr Lazarus McCarthy Chakwera, President of the Republic of Malawi, has assured Malawians that events sorrounding the tragic plane accident that killed the late Right Honourable Dr Saulos Klaus Chilima and eight others, will be thoroughly investigated to determine the cause.

He was speaking at Bingu National Stadium on Sunday where multitudes of gloomy faces had gathered for a State Funeral Ceremony for late Chilima.

Chakwera at the State Funeral



In his remarks, the Malawi leader told the gathering that Government has asked foreign experts to assist in the investigation.

“Ine ndili ndi mafunso omwenso Amalawi Ali nawo kamba koti name sindikumvetsa chimene chinachititsa ngozi ya ndegeyi. ( I have so many unanswered questions just like all Malawians as to what really caused the plane crash),” he emphasized.

“Ndikukupemphani Amalawi tipitilize kusunga mtendere kuti kafukufuku wapadera achitike bwino. ( I ask you my fellow Malawians, to keep calm, so that special investigation related to the plane crash is carried out successfully).”

President Chakwera also assured Malawians that Government will take advantage of the outcome of the investigation to correct the anomalies and avoid repetition of the accident in future.

Secretary to the President and Cabinet (SPC) Collen Zamba said Chilima was a fighter who worked so hard to develop the country.

Philip Isdor Mpango, Tanzania  Vice President described Chilima as an agent of unity and transformation of Malawi’s economy.

Archbishop George Desmond Tambala, who is also the President of Episcopal Conference of Malawi(ECM), said Chilima taught the country to believe in the impossible.

In his remarks, former Kenya Prime Minister Raila Odinga said Chilima stood with the people of Malawi and ensured that democratic principles are upheld all the times.

Representing the United Nations Secretary General, Rebecca Adda Dontoh says Malawi has lost a great leader who helped a lot in the development agenda of the country.

United Transformation Movement (UTM) Secretary General Patricia Kaliati said Chilima wanted Malawians to be self reliant.

Former Attorney General Chikosa Silungwe said Chilima performed perfectly well in the public service through his professionalism.

Son to the late Chilima, Sean said his dad was a leader with vision.

A family representative Ben Chilima thanked everyone that helped in the search for Chilima and others in Chikangawa Forest after the plan crashed.

Dr. Lazarus Chakwera: Malawi’s Strongest President in Times of Tragedy

By Staff Reporter


In the annals of Malawi’s history, Dr. Lazarus Chakwera stands out as a figure of resilience and unity. His presidency, marked by a succession of unprecedented challenges, has revealed his strength and unwavering commitment to the nation. Since assuming office in June 2020, Dr. Chakwera has faced a litany of crises, from the devastating COVID-19 pandemic and destructive cyclones to a severe cholera outbreak, and now, the tragic loss of Vice President Dr. Saulos Chilima. Yet, in every instance, he has risen to the occasion, uniting Malawians and steering the country through each storm.


Navigating the Storms

Dr. Chakwera’s tenure began amidst the global COVID-19 pandemic, a crisis that tested the mettle of leaders worldwide. His administration’s swift response, including public health campaigns, vaccine rollouts, and economic relief measures, demonstrated a commitment to protecting Malawians and mitigating the virus’s impact. This period also showcased his ability to inspire unity and resilience in the face of fear and uncertainty.

President Chakwera and Madam Chakwera

The subsequent cyclones that battered Malawi’s southern regions brought further hardship. The President’s visits to affected areas, coupled with prompt relief efforts and reconstruction plans, provided solace and hope to countless citizens. His leadership during these natural disasters underscored his empathy and dedication to the welfare of all Malawians, reinforcing the spirit of national solidarity.

The cholera outbreak added another layer of complexity to the country’s health challenges. Once again, Dr. Chakwera’s government acted decisively, launching nationwide health campaigns and mobilizing resources to combat the epidemic. These efforts not only curbed the spread of the disease but also strengthened public health systems, showcasing the President’s forward-thinking approach to crisis management.


A Unifying Force in Times of Loss

The recent passing of Vice President Dr. Saulos Chilima has been a profound loss for the nation. In this time of mourning, Dr. Chakwera has emerged as a pillar of strength, offering comfort and stability. His calls for unity and collective prayer reflect his deep-seated belief in the power of communal support and faith. Despite the political undercurrents that often surface during such times, he has maintained a focus on national unity, urging all Malawians to come together in solidarity.

Leadership beyond politics

Dr. Chakwera’s leadership transcends the political arena. His presidency is characterized by a genuine concern for the well-being of the people, a trait that resonates deeply in times of crisis. While some may seek to exploit these tragic moments for political gain, Dr. Chakwera remains steadfast in his mission to unite and uplift the nation. His administration’s resilience and proactive measures have not only navigated Malawi through turbulent times but have also laid the foundation for a more robust and united country.


A Call to Prayer


As Malawi continues to mourn the loss of Dr. Chilima, it is imperative to heed Dr. Chakwera’s call for unity and prayer. In supporting our leaders through prayer, we reinforce the spirit of togetherness that is crucial for overcoming adversity. Dr. Chakwera’s presidency reminds us that true strength lies in unity, compassion, and a shared commitment to the common good.
Dr. Lazarus Chakwera’s tenure as President of Malawi is a testament to strong, empathetic leadership. In the face of relentless challenges, he has united the nation, demonstrating resilience and unwavering dedication. As we navigate these difficult times, let us continue to support and pray for our leader, ensuring that the spirit of unity and strength he embodies continues to guide Malawi towards a brighter future.