Monday, June 23, 2025
No menu items!
spot_img
Home Blog Page 858

Inkosi Gomani yapempha bata pa nthawi ya Maliro a Chilima

0

By Linda Kwanjana

Inkosi ya Makhosi Gomani apempha bata pamene Malawi apitilira kukhuza imfa ya Malemu Dr Saulos Klaus Chilima

Mfumu yaikulu ya Maseko Ngoni Inkosi ya Makhosi Gomani 5 yapempha bata ndi mtendere mdziko muno pamene dziko la Malawi likupitilira kukhuza imfa ya yemwe adali wachiwiri kwa Mtsogoleri wadziko lino a Dr Saulos klaus Chilima.

Gomani Kuyankhula pa mwambo wa Maliro a Chilima



Pempholi ladza pamene achinyamata wena usiku wathawu akhala akugenda magalimoto osiyana siyana pamene amapita kuperekeza a Chilima.

Mukulankhula kwawo ku Nsipe , Ntcheu pa mwambo operekeza a Chilima, a Gomani adati ndikofunika kwambiri kusunga bata chifukwa malemu Chilima adali munthu okonda mtendere.

Mfumu yaikulu Gomani idati Maseko Ngoni yataya munthu ofunika kwambiri omwe udali mzati waukulu mboma la Ntcheu komanso dziko lonse la Malawi.

Mfumu Gomani adati a Chilima adzawakumbukira ngati munthu munthu oopa Chauta komanso okonda banja lake.

Cars On Funeral Convoy Caught in Stone-Throwing Incident at Lizulu Amidst Mourning for VP Saulos Chilima

0


By Burnett Munthali

In a distressing turn of events, several cars including a Toyota Raum bearing license plate DA 9957 became entangled in a stone-throwing incident at Lizulu on Sunday evening 16 June 2024, as emotions ran high in response to the passing of Vice President Saulos Chilima. According to a video which has gone viral on social media, there were no casualties in the car.

The incident occurred amidst mourning and preparations for the VP’s funeral, reflecting the deep emotional impact his death has had on the community. The United Transformation Movement (UTM) has responded with a call for calm and restraint, urging its followers and the public to refrain from acts of violence or destruction during this sensitive time.

The UTM condemns the violence and emphasizes the need for respectful mourning. It underscores the importance of unity and solidarity in honoring Vice President Chilima’s memory, advocating for peaceful expressions of grief.


As the nation navigates this period of mourning, the UTM reaffirms its commitment to supporting Vice President Chilima’s family and ensuring that the funeral proceedings proceed with dignity and respect. It urges its members to uphold the values of compassion and unity, embodying the principles that Vice President Chilima stood for during his tenure.


The stone-throwing incident involving the Toyota Raum DA 9957 at Lizulu serves as a stark reminder of the raw emotions surrounding Vice President Chilima’s passing. The UTM’s message calls for healing and unity as Malawi mourns the loss of a respected leader, urging all to reflect on his legacy with reverence and dignity.

Tragedy Strikes Ahead of VP Saulos Chilima’s Funeral: 4 Dead, 12 Injured in Ntcheu Accident

0


By Burnett Munthali

In a heartbreaking turn of events, tragedy has struck the community of Ntcheu as Malawi prepares for the funeral ceremony of Vice President Saulos Chilima. Reports indicate that a devastating accident has claimed the lives of four individuals and left twelve others including a pregnant woman injured on Sunday 16 June 2024 as the funeral procession was on its way to Nsipe.

The accident, occurring amidst preparations for the solemn ceremony, has cast a shadow over the already somber atmosphere. The United Transformation Movement (UTM) has issued a heartfelt response, urging its followers and the public to remain calm and unified during this challenging time.

UTM secretary general Kaliyati

The UTM’s message emphasizes the importance of compassion and support for the families affected by the accident. It calls for solidarity among its members and the broader community as efforts are made to assist the injured and console the grieving.

Furthermore, the UTM reaffirms its commitment to providing updates and guidance to its members regarding any developments related to the accident and the funeral proceedings. The movement encourages everyone to prioritize safety and respect during this sensitive period.


In conclusion, as Malawi prepares to bid farewell to Vice President Saulos Chilima, the nation is reminded of the fragility of life and the importance of unity in times of adversity. The UTM’s message serves as a beacon of strength and compassion, urging calmness and support amidst tragedy, as the community rallies together to honor the memory of a respected leader.

A DPP akufuna kubweletsa chisokonezo poyika m’bale wathu Saulos Chilima- Zatero Mbadwa Zokhudzidwa

0

By Joseph Banda

Gulu lina lomwe likuzitchula kuti ‘Mbadwa Zokhudzidwa’ lati chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) chamema achinyamata ena omwe chikufuna kuti akayambitse chisokonezo mawa lino pa mwambo oyika m’manda thupi la yemwe anali wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko Dr. Saulos Chilima kumudzi kwawo ku Ntcheu.

Kudzera mchikalata chomwe ife taona, gululi lati lili ndi umboni onse pa izi.

“Ife monga Mbadwa Zokhudzidwa, tikufuna kuima pamodzi ndi mtundu onse wa Malawi pamodzi ndi Mtsogoleri wa dziko lino Dr. Lazarus Chakwera polira abale ndi alongo Including the Vice President Rt. Honourable Dr Saulos Klaus Chilima, amene ataya miyoyo yawo pangozi ija ya ndenge imene idachitika pa 10 June 2025 Ku Chikangawa.

Mbadwa zokhudzidwa



“Ife Mbadwa Zokhudzidwa tapezapo zinthu zingapo zimene ngati sitingalankhulepo ndiye kuti sitichita bwino pofuna kulemekeza moyo ndi Khalidwe la Dr. Saulos Klaus Chilima zomwe adaonesa pokhala dziko lapansi lino.

“Ndizomvetsa chisoni komanso zochititsa manyazi kuti pali anthu ena andale, maka maka a DPP omwe akufuna kutchukilapo pa maliro a Saulos Chilima. Tilinawo umboni okwanila ndipo tikudziwa anthu onse a DPP omwe akupereka ndalama kwa anyamata kuti akanyazitse President Chakwera ku maliro a Chilima ku Nsipe mawa.

“Tawawona akujijilika ku siwa kufuna kukhala ngati kuti amamukonda Saulos pomwe ndiwomwewa amamunyoza, kumunyazitsa, kumutukwana Saulos.

“Pano watisiya, akufuna akhale angelo.
Ife ngati Mbadwa Zokhudzidwa tapeza kuti azipani zotsutsa afuna kuti apangirepo ndale zawo pa Maliro amene agwera dziko lino,” latero gululi mchikalata chake.

Gululi lati laonapo ma audio clip akutuluka kuchokera kwa a  Ntanyiwa a Limpopo FM omwe amakhalira ku dziko la South Africa namakamba nkhani zamabodza ndikufuna kuononga mbiri ya anthu ena kuphatikizapo mtsogoleri wadziko lino motumidwa ndi a zipani zotsutsa amene amakatengako ndalama kudzera kwa munthu wina amene amakhala ku South Africa koma adali mugawo limodzi la chitetezo Cha Mtsogoleri wakale  wadziko lino  Prof Arthur Peter Mutharika.

“Iyeyo amalumikiza ma wire pakati pa anthu aku DPP ndi Limpopo FM.
Anthuwa akungofuna kudzetsa mkwiyo kwa mzika za Malawi ponena zinthu za mkutu. Mbadwa Zokhudzidwa zapeza kuti a zipani zotsutsa ndiwo akhala akukolezera kuti a Chipani Cha UTM azipanga zithu mokwiya poperekera zida kuti anthu adziyimba nyimbo zonyoza a Chakwera zomwe sizingakondwereste mzimu wa Dr. Chilima.

“Dr. Chilima adali mkatolika weni weni osachita nawo mapokoso opanda mzeru.

“Mbadwa Zokhudzidwa zapeza kuti a zipani zotsutsa apeza njira yofuna kutchukirapo muzipani zawo pofuna kubweresa mabodza ochuluka kuti anthu adane ndi a Chakwera.

“Tamva kuti akufuna kuti a Peter Mutharika akapita ku maliro asakagwirane chanza ndi aliyense kapena kumwa madzi amene akapatsidwe ati angakawaphe. Za ziii zeni zeni. Mutharika amapita ku maliro?

“Tikudziwa kuti zonsenzi mkufuna kupeza zifukwa zoti asakapezeke ku Maliro a Dr. Chilima. Koma a Malawi akudziwa kale kuti inu simupita ku Maliro,” chaonjezera chotele chikalatachi.

Ndipo chapitiliza kunena kuti :”Imfa ya Dr.Justin Malewezi amene adakhalapo Vice President wa dziko lino la Malawi mu utsogoleri wa Dr. Bakili Muluzi APM adabwera?

“Maliro a mayi Annie Muluzi Mayi awo a Dr. Atupele Muluzi, amene adali running mate wanu mu 2019, mudabwera?

“Maliro Vice President wanu Dr. Goodal Gondwe, mudakakamizidwa tsiku lomaliza pomwenso mudakafika mochedwa osawona nkhope.

“Maliro senior chiefs mdziko muno including a Chimaliro aku Thyolo kumene amacholera APM, mudapita?  Mdziko muno mudachitika maliro a senior Chief Kapoloma amene adali related to former President wa dziko lino Dr Bakili Muluzi ku Liwonde koma a Peter Mutharika okhalira ku Mangochi sadapezeke so.

“Chimene chikhale chachilendo ndi chiti kuti APM akalephere kupita ku maliro a Dr Klaus Chilima

“Dr Saulos Klaus Chilima sadali munthu amene amachitidwa provoke so easily and react to carelessly.

“Mulemekezeni. Wakhala moyo wa chete kuchokera pamene Chipani Cha DPP chidakhala chikumuchita provoke. Mwachitsanzo adayankhapo munthawi Ina pamene a DPP adamuyamba ndikunena kuti iye ngosayamika.
Adayankha nanena kuti musati ndine osayamika chifukwa sindikuyenera kukhala ineyo okuyamikani chifukwa ndidakupezani ku opposition ndikukulowetsani m’boma, so mukuyenera kundiyamika ndi Inuyo.

“A DPP adamuchita provoke namanena kuti adamutenga akugulitsa yabooka ndipo amutsuka tsuka. A DPP adatenga mzimayi amene adachita video clip nkuwuza anthu kuti Dr. Saulos Klaus Chilima sadali wa ku Ntcheu koma ku Mozambique.

“Ndipo a DPP adamutchula kuti Iye ndi Zeze not Saulos Klaus Chilima.
Wakoma lero Saulos mumamunyoza uja? Chonde a Malawi a mzanga maka uko ku Ntcheu a Ngoni, tisalore kuti anthu a DPP atigwiritse ntchito yosokoneza maliro a Dr. Chilima.

“Mulemekezeni m’bale wanu kuti mzimu wake uwuse mu mtendere.”

DPP Spokesperson dismiss fake letters to AFORD President Enoch Chihana

0


By Burnett Munthali


Tensions in Malawi’s political scene have escalated following the Democratic Progressive Party’s (DPP) strong denouncement of letters allegedly authored by the Malawi Congress Party (MCP). These letters purportedly warned AFORD President Enoch Chihana about potential actions that could undermine MCP’s political interests. This controversy underscores the intricacies of political maneuvering and alliances as parties gear up for future electoral battles.


Both the DPP presidential candidate and spokesperson have vehemently criticized the letters attributed to MCP. They dismiss them as manipulative attempts to interfere in AFORD’s internal affairs and sow discord among opposition parties. According to DPP officials, such tactics not only jeopardize the spirit of fair competition but also undermine efforts to build a united front against the ruling party.

Namalomba

DPP representatives have framed MCP’s alleged actions as indicative of desperation to consolidate power and influence within opposition ranks. They argue that these maneuvers aim to weaken solidarity among opposition parties, thereby potentially benefiting the ruling party in upcoming elections.

The controversy has sparked diverse reactions from the public and political observers. Supporters of MCP may see the letters as legitimate efforts to protect party interests, while critics view them as divisive and detrimental to broader opposition unity. The incident has prompted calls for transparency and ethical conduct in political engagements to uphold democratic principles.


As Malawi approaches future elections, the fallout from this controversy could shape electoral strategies and alliances. It underscores the complexities of coalition-building and strategic positioning among political parties, influencing voter perceptions and potential outcomes at the ballot box.


The DPP’s dismissal of MCP’s warning letters to AFORD President Enoch Chihana highlights the competitive nature of Malawi’s political landscape. As parties navigate these challenges, maintaining integrity, fostering unity, and adhering to democratic norms will be crucial in shaping the country’s political future. The unfolding dynamics will continue to shape the narrative leading up to the next electoral cycle, impacting the choices and outcomes for Malawian voters.