Friday, July 4, 2025
No menu items!
spot_img
Home Blog Page 1109

Kagwireni ntchito mwa ukadaulo-Gumba

0

By Chisomo Phiri

Nduna yowona zamalo m’dzikolo muno olemekezeka Deus Gumba apempha achinyamata okwana 353 omwe alembedwa ntchito mu undunawu kuti agwire ntchito mwa ukadaulo ndimozipeleka kuti kusamvana pa nkhani zamalo komwe kumachitika m’madera ambiri m’dziko muno kuthe.

A Gumba amayankhula izi lachiwiri mu mzinda wa Blantyre komwe amakhazikitsa maphunziro omwe achinyamatawa akhale akulandira kwa sabata zinayi kuti adziwe zina mwazofunika zomwe angatsate pomwe akugwira ntchito m’boma.

“Kulimilandu yambiri yokhudza malo kunjaku,tiyeni tikagwire ntchito mwa ukadaulo ndimozipeleka kuti izi zikathe m’madera omwe tikakhale tikugwiramo ntchito. Tikudalira inu kuti ndizotheka,” anatero a Gumba.

Iwo anatiso achinyamatawa akepewe mchitidwe waziphuphu pomwe akugwira ntchito zawo poti izi zimabwezeletsa chitukuko m’mbuyo.

“Ziphuphu zimabwezeletsa chitukuko m’mbuyo. Kapeweni kuchita mchitidwe waziphuphu m’magwiridwe anu a ntchito,” anatsindika a Gumba.

Malinga ndi a Gumba, achinyamata 353 omwe boma lalemba mu unduna wawo ndimbali imodzi yoonetsetsa kuti achinyamata akupeza ntchito mdziko muno monga m’tsogoleri wadziko lino Dr. Lazarus Chakwera analonjezera asanalowe m’boma.

M’mawu ake,mkulu wa sukulu ya Malawi School of Government yomwe ikupeleka maphunzirowa kwa achinyamatawa a Professor Asiyati Chiweza anati ayesetsa kuti achimatawa aphunzire ndondomeko zonse zoyenera kutsata pomwe akhale akugwira ntchito m’boma.

“Ngakhale nthawi yoti aphunzire ikuoneka yochepa koma monga akadaulo popeleka maphunziro akagwiridwe kantchito m’boma, tiyesetsa kuti achinyamatawa asulidwe bwino lomwe ndikuti akathe kugwira ntchito bwino ndimotumikira amalawi.

“Ndizambiri ataphunzire kuno, zina mwaizo ndimonga chikhalidwe cha anthu ogwira ntchito m’boma ndi zina zofunika,” anatero a Chiweza.

Mwa achinyamata 353 wa, achinyamata 34 akuyembekezeka kukhala m’makhonsolo a m’maboma onse m’dziko muno pomwe achinyamata okwana 319 akuyembekezeka kumakagwira ntchito zokhudza malo mothandizana ndimafumu akuluakulu m’maboma onse m’dziko muno.

Achinyamatawa anasankhidwa kuchokera boma lililonse m’dziko muno.

MHEN yalimbikitsa kufunika kogwila ntchito za umoyo ndi anthu amagulu onse

0

By Wilfred Golden

Bungwe la Malawi Health Equity Network (MHEN) lati kupezeka kwa anthu amagulu osiyanasiyana m’magulu a amayi omwe amagwila ntchito za umoyo mongodzipeleka m’madela (Mother Care Groups), kukulimbikitsa ntchito yawo yofuna kufikila paliponse ndi uthenga wa kufunika kolondoloza katemela kwa ana osapitilila zaka zisanu.

Wayakhula izi ndi m’modzi mwa omwe akuyendetsa ntchitoyi ku MHEN David Samikwa pomwe anakayendela gulu la amayiwa kwa Sathe m’boma la Lilongwe ndipo iye anati chikhazikitsileni maguluwa anthu ambiri afikilidwa ndi uthengawu kaamba koti panali kulumikizana pa magulu onse.



“M’magulu amenewa timalimbikitsa kuti muzikhala anthu abizinezi, amipingo, atsogoleli a m’dela komanso achinyamata mwa ena, ndipo izi zikuthandizila kuti anthuwa adzitha kufikilana ndikumalimbikitsana mosavuta potengela kuti amadziwa momwe angathe kufikilana molingana ndi mbali yawo,” Samikwa anatelo.

Cholinga cha magulu amenewa komanso mikumanoyi ndichofuna kupititsa patsogolo ntchito yozindikilitsa amayi kufunika kolondoloza akatemela onse kwa ana.

MHEN ikuchita mikumano ndi magulu a amayiwa ku Lilongwe kwa sabata ziwiri pofuna kuchita kalondolondo pa momwe ntchitozi zikuyendela kuyambila nthawi yomwe maguluwa anakhazikitsidwa m’chaka cha 2018.

Mwa makomiti ena omwe akugwila nawo ntchitozi m’madela ndi monga Village Development Committes, Parent Teachers Association, Area Development Committees.

Ndondomekoyi ikuchitika pansi pa thandizo lomwe likupelekedwa ndi bungwe la Global Alliance Vaccine Immunization (GAVI) ndi ukadaulo kuchokela ku unduna wa za umoyo.

Opinion: What is the impact of devaluation in Malawi today and years to come?

By Burnett Munthali

The theory of devaluation is that it occurs when a country creates a downward adjustment of its currency value to balance trade. Devaluing a currency reduces the cost of a country’s exports and makes imports less attractive. As exports increase and imports decrease, there is typically a better balance of payments as the trade deficit shrinks.

Impact

Devaluation can result in an increase in the prices of products and services over time. The increase in the price of imports causes consumers to purchase their goods from domestic industries. The amount of the price increases, however, is dependent on the competition of supply and aggregate demand. In a more confusing manner, Malawi is experiencing the rising cost of living in both domestic products and imports. A packet of sugar has now risen to MWK2, 750 in Chipiku Stores, one of the cheapest chain stores throughout the country.

Devaluing a currency is usually an economic policy, whereby devaluation makes a currency weaker compared to other currencies, which would boost exports, close the gap on trade deficits, and shrink the cost of interest payments on government debt.

Does Malawi have good reasons for devaluing its currency?

Reserve Bank of Malawi

Malawi’s Official Reserves Are Now Less Than $300 Million

The latest devaluation is aimed at correcting supply-demand imbalances and countering arbitrage opportunities that have arisen in the market, according to a statement signed by Governor Wilson Banda.

As such, exchange rate devaluation (depreciation) tends to raise the price of locally manufactured goods and services, thus invokes imported inflation. Unfortunately, Malawi doesn’t have manufacturing industries and the country continues to depend on importation of goods from outside thereby solving nothing at the end of this economic equation.

The disadvantages of depreciating exchange rate is that it can cause foreign imports to appear more expensive on domestic markets, and decrease purchasing power in foreign markets. This can encourage domestic consumption but that is not always possible if some goods simply are not available domestically. However, in the case of Malawi, everything is becoming very expensive. In fact, I even wonder that local products are the ones that are more expensive than imported goods.

Conclusion

In May 2022, the Malawian kwacha was devalued up to 25 percent against the U.S. dollar, a development the central bank governor said would “allow the exchange rate to adjust to a market-determined clearing position with a view of endorsing a flexible exchange rate that reflects market fundamentals.”

In what government said they would like to help address macroeconomic challenges, the Reserve Bank of Malawi devalued the national currency, the Malawi kwacha, by 44 percent in early November 2023; as of 24 November, the Malawi kwacha was trading at MWK 1 685/USD 1, compared to MWK 1 116 in late October 2023.

By devaluing its currency, a country makes its money cheaper and boosts exports, rendering them more competitive in the global market. Conversely, foreign products become more expensive, so the demand for imports falls. Governments use devaluation to combat a trade imbalance and have exports exceed imports. But which exports are being boosted on the global market for Malawi? Obviously, the answer is zero. Has the demands for imports fallen in the country? The demand for imports continues to rise in Malawi, the country keeps importing more and more while we are failing to manufacture and export.

Women’s Rights Activists Unite In Support of Esther Jolobala’s Demand For Uladi Mussa’s Remarks Apology

0

By Twink Jones Gadama

Member of Parliament for Machinga East, Esther Jolobala has strongly criticized Uladi Mussa for his derogatory remarks targeting women while joining the ruling Malawi Congress Party (MCP).
. Jolobala has called on Mussa to retract his words and apologize for his irresponsible behavior.

During Mussa’s induction into the MCP, he told the gathering that “I was suspended for nine months and I wouldnt be waiting for nine months as am pregnant, waiting for the baby.”
Hid derogatory comments likening his defection to the party to being pregnant and waiting for the baby compelled Jolobala to react.

Esther Jolobala

Jolobala, along with numerous women and gender rights activists, viewed these remarks as highly insulting and demeaning to women.

Jolobala, who firmly believes in promoting gender equality and women’s rights, stated that Mussa’s comparison was disrespectful and unacceptable. She emphasized that women’s experiences during pregnancy are not comparable to political situations and should never be used in such a context. Jolobala called on Mussa to acknowledge the inappropriateness of his comments and offer a sincere apology to all the women who were offended.

However, when approached for comments on the matter, Mussa refused to respond, leaving the public in uncertainty regarding his stance on the issue. Jolobala, though disappointed by Mussa’s silence, assured that appropriate action would be taken if he fails to rectify his mistake.

While the course of action remains undisclosed for now, Jolobala affirmed that the necessary steps would be announced in due time. She firmly believes that it is crucial to address such instances of misogyny and disrespectful behavior, particularly in the political realm, where leaders should set an example for the nation.

Jolobala further asserted that politics and actual phenomena should not be interlinked, emphasizing the need for politicians to be conscious of their language and its impact on the public. As representatives of the people, elected officials must demonstrate respect, equality, and sensitivity in their words and actions.

The incident involving Auladi Mussa’s remarks has sparked a debate on gender equality within the political landscape of Malawi. Women’s rights activists and concerned citizens have voiced their support for Jolobala’s call for an apology and expectation for appropriate consequences if Mussa fails to comply.

The incident serves as a reminder that derogatory remarks, particularly those that perpetuate harmful stereotypes, have no place in today’s society. As the nation progresses towards a more inclusive and egalitarian future, it is essential for leaders to lead by example and ensure that their words foster respect and unity, rather than division and discrimination.

Ultimately, the demand for Auladi Mussa’s apology underscores the importance of holding elected officials accountable for their words and actions, ensuring that they uphold the principles of equality and dignity for all citizens, regardless of gender.

Concerned Clergy Argues Proposed Age limit Legislation Discriminates Against Elders

0

By Twink Jones Gadama

In a resounding call for fairness and inclusivity, a group of concerned clergy has urged members of parliament to refrain from tabling an age bill that they argue is discriminatory against elders.

Led by prominent clergyman Steve Chimwaza, the group criticized the decision to introduce legislation without proper consultation and labeled the politics of tit-for-tat as archaic and retrogressive.

Parliament, to table age bill?

With their voices amplified by a growing public outcry, the clergy’s plea highlights their unwavering commitment to ensure all voices are heard and respected in matters of legislative importance.

Emblematic of their dedication, Chimwaza announced that clergy members would converge at parliament to voice their concerns with the proposed bill.

The crux of the clergy’s opposition lies in their assertion that the age bill, as currently proposed, lacks the necessary consultation required for a fair representation of the broader population.

According to Chimwaza, the individual responsible for introducing the bill failed to seek input from relevant stakeholders before drafting it, thereby excluding crucial perspectives.

“It is not acceptable to table legislation with an eye on someone,” Chimwaza stated. “The politics of tit for tat are archaic and retrogressive.

As clergy, we must ensure that the voices of the marginalized are always considered and that legislation reflects the needs and aspirations of the people it seeks to serve.”

This call for consultation extends beyond the clergy and resonates with many citizens who share the concerns surrounding the current age bill.

In a society that values inclusivity and diversity, the clergy’s efforts have energized the ongoing debate around the fairness of the proposed legislation.

The move by the concerned clergy to take their concerns directly to parliament demonstrates their commitment to engaging in constructive dialogue and striving for a more democratic process.

As Chimwaza emphasized, the absence of consultation undermines the legitimacy of any legislation and disregards the principles of representative governance.

Informed by their deep-rooted moral compass, the clergy’s advocacy for fair legislation is part of a larger narrative driving positive change within society.

By questioning the legitimacy of the age bill and advocating for more inclusive decision-making processes, the clergy reinforces the core values of respect, equity, and justice.

As the date of their scheduled gathering approaches, the clergy’s mobilization serves as both a warning to lawmakers and an inspiration to citizens. By standing up against discriminatory legislation, the clergy hopes to prompt a critical reflection among parliamentarians, leading to improved legislation that genuinely represents the interests of all citizens.

In a time where the ability to work collaboratively and inclusively is paramount, the clergy’s call for consultation and fairness sends a powerful message.

Their efforts signify that the path to a fairer society is paved with dialogue, understanding, and a commitment to hearing and respecting all perspectives.