Friday, May 8, 2026
No menu items!
spot_img
Home Blog Page 661

Boma laletsa kuyitanitsa kunja katundu wina wopezeka m’dziko lino

0

By Burnett Munthali

Boma laletsa kuyitanitsa kunja katundu pafupifupi 20 yemwe uli wopezeka m’dziko muno.

Kalata yochokera kuboma yotsimikiza chiletsochi yati lamuloli layamba kugwira ntchito kuyambira lero.

Mwa katundu wina yemwe boma laletsa kuyitanitsa kuchoka kunja akuphatikizapo masamba ndi zipatso, kupatulapo zomwe sizimamera m’dziko muno.

Wolemekezeka a Vitumbiko Mumba

Katundu wina omwe waletsedwa ndi ufa, mazira, mpunga, totokosera mano, zikolopa, ndi mipando yokhomedwa kunja.

Mkaka ndi katundu wina yemwe wagwera pa ndondomeko ya zinthu zomwe sizingayitanitsidwe kunja.

Nduna yowona za malonda a Vitumbiko Mumba yatsimikizira za chiletsochi pa tsamba lawo la Facebook.

Mumba wati chiletsochi chayamba kugwira ntchito nthawi yomweyo ndipo ali ndi cholinga chothandiza kupanga katundu m’dziko muno.

Iye wati chiletsochi chingathandize kulimbikitsa bizinesi za m’dziko lino komanso kuchepetsa kudalira zinthu zochokera kunja.

Boma lati lamuloli lipindulitsa anthu amene amapanga katundu m’dziko muno kuti apeze msika wotakata.

Nduna ya malonda yati sipadzakhala kusintha pa chiletsochi ndipo boma lidzaonetsetsa kuti likutsatiridwa.

Mumba wati kuphwanya lamuloli kudzakhala ndi chilango cholemetsa kwa onse omwe adzapezeke akuphwanya ndondomekoyi.

Otsatira ndondomekozi akuyembekezera kuti chiletsochi chingathandize kukweza chuma cha dziko.

Anthu ambiri akuyembekezera kuti lamuloli lidzathandiza amalonda ang’onoang’ono omwe amakumana ndi mpikisano waukulu kuchokera kwa amalonda akuluakulu ochokera kunja.

Ena mwa amalonda ati akuyembekezera kuti boma likhazikitse njira zothandizira kuti kupanga katundu m’dziko muno kukhale kopindulitsa.

Nduna ya malonda yati boma lipitiliza kutsatira ndondomeko zokhudza chitukuko cha bizinesi za m’dziko muno.

Iye watsimikizira kuti zinthu zomwe sizipezeka m’dziko muno zidzapitirizabe kuyitanitsidwa kunja popanda zovuta.

Mumba wapempha anthu komanso mabungwe ogwira nawo ntchito kuti athandizire kutsatira ndondomekozi.

Iye wati boma likufuna kuona kuti dziko limapindula ndi chuma chake pogwiritsa ntchito zinthu zomwe zilipo m’dziko muno.

Mumba watsiriza ponena kuti ndondomekoyi ndi yofunika kwambiri kuti dziko lipitirire kulimbikitsa chuma chake.

Allan joins Bankers

0



By Chisomo Phiri

Reigning TNM Super League champions Silver Strikers have made a significant addition to their squad, securing the services of prolific striker Emmanuel Allan.

The former Moyale Barracks goal-scorer inked a three-year deal with the Bankers on Friday, marking the team’s fifth signing in the current transfer window.

Emmanuel Allan


He joins a talented crop of new recruits at the club, including striker Samuel Adebiyi Adeyemi, defender Precious Sambani, and midfielders Festus Duwe and Felix Demakude.

Allan’s impressive form in the 2024 season, where he played for Moyale Barracks, caught the attention of Silver Strikers’ scouts.

His nine-goal haul in the FDH Bank Cup earned him the Golden Boot award, cementing his reputation as a clinical finisher.

Imperial Motors unveils sixth-generation Mitsubishi Triton

0

By Chisomo Phiri

Imperial Motors made a splash on Thursday night with the launch of the cutting-edge sixth-generation Mitsubishi Triton which has Artificial Intelligence-powered features that redefine the driving experience, making mobility easier and safer for travelers.

The new Mitsubishi Triton takes innovation to the next level, allowing drivers to use their mobile phones to input destinations, while its advanced features automatically assist in avoiding accidents.

In an interview with journalists, the company’s  Chairman Tim Jaques,said the vehicle’s robust new chassis and suspension, crafted with highly flexible materials, absorb road noise and vibrations, ensuring a comfortable and safe driving experience that minimizes stress and fatigue.


On his part, Minister of Trade and Industry Vitumbiko Mumba, who graced the lauch commended Imperial Motors for its unwavering commitment to providing the Malawian market with the latest products.

The Minister also praised the company’s recruitment policy, which prioritizes local talent, noting that Malawians hold key positions within the organization.

Imperial Motors opened its operations in Malawi in 2014.

Mighty Wanderers,Civil Service United in Mozambique for Songo International Tournament

0

By Chisomo Phiri

The country’s football giants Mighty Wanderers and Civil Service United arrived in Tete, Mozambique on Friday evening, ready to participate in the Songo International Tournament.

The tournament kicks off today and will run until Monday.



In the opening match,Wanderers will face off against CD Chingale at Compus Sul Stadium on Saturday, while Civil will take on Unaio Desportivo de Songo.

Both teams are using the tournament as a crucial part of their preseason preparations, ahead of the new season which commences on March 29,2025.

Bushiri’s day of reckoning: Why extradition to South Africa is inevitable

By Jones Gadama

The recent ruling by the Lilongwe Magistrate Court that Prophet Shepherd Bushiri and his wife Mary must be extradited to South Africa to face multiple charges has sparked intense debate.

While some argue that Bushiri is being unfairly targeted, others believe that he must face the music and prove his innocence in a South African court.

As a self-acclaimed prophet, Bushiri’s actions have consequences that go beyond his religious followers.

Bushiri



His alleged involvement in rape, forgery, fraud, and jumping bail are serious crimes that cannot be swept under the carpet.

The fact that he has been contributing to Malawi’s development through his various business ventures, including the construction of Goshen City, is commendable, but it does not grant him immunity from prosecution.

The Bible teaches us that doing God’s will often comes with persecution and hatred from the world. However, this should not be used as a justification for Bushiri to resist extradition and evade justice.

Instead, he should take this opportunity to clear his name and demonstrate his commitment to upholding the law.

It is essential to recognize that no one is above the law, regardless of their social status, wealth, or influence.

The rule of law is a fundamental principle of any democratic society, and it must be applied equally to all citizens.

By resisting extradition, Bushiri is not only undermining the rule of law but also perpetuating a culture of impunity.

Furthermore, the South African government has expressed concerns about Bushiri’s lack of cooperation and his attempts to evade justice.

Justice Minister Mmamoloko Kubayi has stated that the government is ready to oppose any appeal by Bushiri and ensure that he faces trial in South Africa.

Bushiri’s extradition to South Africa is not only inevitable but also necessary to uphold the rule of law and ensure that justice is served. His contributions to Malawi’s development are appreciated, but they do not excuse his alleged crimes. By facing trial in South Africa, Bushiri has the opportunity to clear his name and demonstrate his commitment to upholding the law.

As the Bible teaches us, doing God’s will often comes with challenges and persecution.

However, it is how we respond to these challenges that defines our character and commitment to justice.

Bushiri’s decision to resist extradition and evade justice is a test of his character, and it is essential that he makes the right choice.